Bingu wa Muntharika
From Wikipedia
Bingu wa Mutharika, amene anabadwa pa 24 Febuluale 1934, ndi kachenjede wa zachuma (economist), mtsogoleri wa ndale ndiponso Pulezidenti wa dziko la Malawi. A Mutharika anakhala Pulezidenti pa 24 Meyi mchaka ka 2004 pamene anapambana pa chisankho cha Pulezidenti.