Masauko Chipembere

From Wikipedia

Jump to: navigation, search

Henry Masauko Blasius Chipembere (5 August 1930 - 24 September 1974) anali mmodzi wa anthu amene anafuna kuti anthu a ku Malawi adzilamulire okha komanso anali mphunzitso wa mbiri ku Universty ya UCLA.

[edit] Ntchito

Ngati mmodzi wa anthu amene ankakhulupilira kuti anthu a ku Malawi adzilamulire paokha, a Chipembere anali mmodzi wa anthu a chipani cha ]]Nyasaland African Congress]], wachiwiri wa woyang'anira boma la Domasi komanso . Dziko la Nyasaland litalandira ufulu wodzilamulira iwo anali msungichuma wa chipani cha Malawi Congress Party ndi nduna yoyang'anira za maboma aang'ono komanso nduna ya maphunziro.


[edit] Source

Personal tools